Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 88:16 - Buku Lopatulika

16 Kuzaza kwanu kwandimiza; zoopsa zanu zinandiononga.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Kuzaza kwanu kwandimiza; zoopsa zanu zinandiononga.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Mkwiyo wanu wandimiza, moyo wanga waonongekeratu ndi ukali wanu woopsa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Ukali wanu wandimiza; zoopsa zanu zandiwononga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 88:16
13 Mawu Ofanana  

Anditembenuzira zondiopsa, auluza ulemu wanga ngati mphepo; ndi zosungika zanga zapita ngati mtambo.


chifukwa cha ukali wanu ndi kuzaza kwanu; popeza munandinyamula ndipo munandigwetsa.


Thupi langa linjenjemera ndi kuopa Inu; ndipo ndichita mantha nao maweruzo anu.


Mudzabisala kosatha kufikira liti, Yehova; ndi kuzaza kwanu kudzatentha ngati moto kufikira liti?


Adziwa mphamvu ya mkwiyo wanu ndani, ndi ukali wanu monga ayenera kukuopani?


Pakuti tionongeka mu mkwiyo wanu; ndipo m'kuzaza kwanu tiopsedwa.


Anachotsedwa ku chipsinjo ndi chiweruziro; ndipo ndani adzafotokoza nthawi ya moyo wake? Pakuti walikhidwa kunja kuno; chifukwa cha kulakwa kwa anthu anga Iye anakhomedwa.


Ndipo atapita masabata makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri wodzozedwayo adzalikhidwa, nadzakhala wopanda kanthu; ndi anthu a kalonga wakudzayo adzaononga mzinda ndi malo opatulika; ndi kutsiriza kwake kudzakhala kwa chigumula, ndi kufikira chimaliziro kudzakhala nkhondo; chipasuko chalembedweratu.


Iye amene sanatimane Mwana wake wa Iye yekha, koma anampereka chifukwa cha ife tonse, adzalekeranji kutipatsanso ife zinthu zonse kwaulere pamodzi ndi Iye?


Khristu anatiombola ku temberero la chilamulo, atakhala temberero m'malo mwathu; pakuti kwalembedwa, Wotembereredwa aliyense wopachikidwa pamtengo.


chifukwa lafika tsiku lalikulu la mkwiyo wao, ndipo akhoza kuima ndani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa