Masalimo 88:16 - Buku Lopatulika16 Kuzaza kwanu kwandimiza; zoopsa zanu zinandiononga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Kuzaza kwanu kwandimiza; zoopsa zanu zinandiononga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Mkwiyo wanu wandimiza, moyo wanga waonongekeratu ndi ukali wanu woopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ukali wanu wandimiza; zoopsa zanu zandiwononga. Onani mutuwo |
Ndipo atapita masabata makumi asanu ndi limodzi mphambu awiri wodzozedwayo adzalikhidwa, nadzakhala wopanda kanthu; ndi anthu a kalonga wakudzayo adzaononga mzinda ndi malo opatulika; ndi kutsiriza kwake kudzakhala kwa chigumula, ndi kufikira chimaliziro kudzakhala nkhondo; chipasuko chalembedweratu.