Masalimo 88:12 - Buku Lopatulika12 Zodabwitsa zanu zidzadziwika mumdima kodi, ndi chilungamo chanu m'dziko la chiiwaliko? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Zodabwitsa zanu zidadziwika mumdima kodi, ndi chilungamo chanu m'dziko la chiiwaliko? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Kodi zodabwitsa zanu zimadziŵika mu mdima? Ndani angadziŵe za chithandizo chanu chopulumutsa m'dziko la anthu oiŵalika? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kodi zozizwitsa zanu zimadziwika ku malo a mdima, kapena ntchito zanu zolungama ku dziko la anthu oyiwalika? Onani mutuwo |