Masalimo 88:11 - Buku Lopatulika11 Adzafotokozera chifundo chanu kumanda kodi, chikhulupiriko chanu kumalo a chionongeko? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Adzafotokozera chifundo chanu kumanda kodi, chikhulupiriko chanu kumalo a chionongeko? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kodi chikondi chanu chosasinthikacho amachilalikira ku manda? Kodi amasimba za kukhulupirika kwanu ku malo achiwonongeko? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kodi chikondi chanu chimalalikidwa mʼmanda, za kukhulupirika kwanu ku malo a chiwonongeko? Onani mutuwo |