Masalimo 87:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo oimba ndi oomba omwe adzati, akasupe anga onse ali mwa inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo oimba ndi oomba omwe adzati, akasupe anga onse ali mwa inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Oimba ndi ovina adzati, “Ziyoni ndiwe kasupe wa madalitso athu onse.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.” Onani mutuwo |