Masalimo 87:6 - Buku Lopatulika6 Yehova adzawerenga, polembera mitundu ya anthu, uyu anabadwa komweko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Yehova adzawerenga, polembera mitundu ya anthu, uyu anabadwa komweko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Tsono polemba maina a mitundu yonse ya anthu, Chauta adzati, “Wakutiwakuti adabadwira ku Ziyoni.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” Sela Onani mutuwo |