Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 87:1 - Buku Lopatulika

1 Maziko ake ali m'mapiri oyera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Maziko ake ali m'mapiri oyera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Mzinda umene Chauta adamanga maziko ake, uli pa phiri loyera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 87:1
17 Mawu Ofanana  

Pamenepo Solomoni anayamba kumanga nyumba ya Yehova ku Yerusalemu, m'phiri la Moriya, kumene Mulungu anaonekera kwa Davide atate wake pamalo pamene Davide anakonzeratu pa dwale la Orinani Myebusi.


Ndikweza maso anga kumapiri: Thandizo langa lidzera kuti?


Mapazi athu alinkuima m'zipata zanu, Yerusalemu


Monga nswala ipuma wefuwefu kukhumba mitsinje; motero moyo wanga upuma wefuwefu kukhumba Inu, Mulungu.


Muchitiranji nsanje mapiri inu a mitumitu, ndi phirilo Mulungu analikhumba, akhaleko? Inde, Yehova adzakhalabe komweko kosatha.


Ndipo anamanga malo oyera ake ngati kaphiri, monga dziko lapansi limene analikhazikitsa kosatha.


Ndipo adzayankhanji amithenga a amitundu? Kuti Yehova wakhazikitsa Ziyoni, ndipo m'menemo anthu ake ovutidwa adzaona pobisalira.


chifukwa chake Ambuye Yehova atero, Taonani, ndiika mu Ziyoni mwala wa maziko, mwala woyesedwa mwala wa pangodya, wa mtengo wake wokhazikika ndithu; wokhulupirira sadzafulumira.


naonso ndidzanka nao kuphiri langa lopatulika, ndi kuwasangalatsa m'nyumba yanga yopemphereramo; zopereka zao zopsereza ndi nsembe zao zidzalandiridwa paguwa langa la nsembe; pakuti nyumba yanga idzatchedwa nyumba yopemphereramo anthu onse.


Atero Yehova: Ndabwerera kudza ku Ziyoni, ndidzakhala pakati pa Yerusalemu; ndi Yerusalemu adzatchedwa, Mzinda wa choonadi; ndi phiri la Yehova wa makamu, Phiri lopatulika.


Ndiponso Ine ndinena kwa iwe, kuti iwe ndiwe Petro, ndipo pa thanthwe ili ndidzakhazika Mpingo wanga; ndipo makomo a dziko la akufa sadzagonjetsa uwo.


ndipo mau awa ochokera Kumwamba tidawamva ife, pokhala pamodzi ndi Iye m'phiri lopatulika lija.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa