Masalimo 86:14 - Buku Lopatulika14 Mulungu, odzikuza andiukira, ndi msonkhano wa anthu oopsa afuna moyo wanga, ndipo sanaike Inu pamaso pao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Mulungu, odzikuza andiukira, ndi msonkhano wa anthu oopsa afuna moyo wanga, ndipo sanaike Inu pamaso pao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Inu Mulungu, anthu achipongwe andiwukira. Anthu opanda chifundo akufunafuna moyo wanga ndipo sasamala za Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Inu Mulungu wanga, anthu odzikuza akundithira nkhondo; anthu ankhanza akufuna kundipha, amene salabadira za Inu. Onani mutuwo |