Masalimo 84:7 - Buku Lopatulika7 Apita mwamphamvu naonjezapo mphamvu, aoneka pamaso pa Mulungu mu Ziyoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Apita mwamphamvu naonjezapo mphamvu, aoneka pamaso pa Mulungu m'Ziyoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mphamvu zao zimanka zichulukirachulukira. Mulungu wa milungu adzaoneka m'Ziyoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Iwo amanka nakulirakulira mphamvu mpaka aliyense ataonekera pamaso pa Mulungu mu Ziyoni. Onani mutuwo |