Masalimo 84:12 - Buku Lopatulika12 Yehova wa makamu, wodala munthu wakukhulupirira Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Yehova wa makamu, wodala munthu wakukhulupirira Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Inu Chauta Wamphamvuzonse, ngwodala munthu woika chikhulupiriro chake pa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Inu Yehova Wamphamvuzonse, wodala ndi munthu amene amakhulupirira Inu. Onani mutuwo |