Masalimo 78:60 - Buku Lopatulika60 ndipo anachokera chokhalamo cha ku Silo, chihemacho adachimanga mwa anthu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201460 ndipo anachokera chokhalamo cha ku Silo, chihemacho adachimanga mwa anthu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa60 Adasiya malo ake a Silo kumene ankakhala, adasiya hema limene ankakhalamo pakati pa anthu, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero60 Anasiya nyumba ya ku Silo, tenti imene Iyeyo anayimanga pakati pa anthu. Onani mutuwo |