Masalimo 78:59 - Buku Lopatulika59 Pakumva ichi Mulungu, anakwiya, nanyozatu Israele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201459 Pakumva ichi Mulungu, anakwiya, nanyozatu Israele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa59 Pamene Mulungu adamva zimenezi, adakwiya kwambiri, ndipo adakana Aisraele kotheratu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero59 Pamene Mulungu anamva zimenezi, anakwiya kwambiri; Iye anakana Israeli kwathunthu. Onani mutuwo |