Masalimo 78:49 - Buku Lopatulika49 Anawatumizira mkwiyo wake wotentha, kuzaza, ndi kupsa mtima, ndi nsautso, ndizo gulu la amithenga ochita zoipa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Anawatumizira mkwiyo wake wotentha, kuzaza, ndi kupsa mtima, ndi nsautso, ndizo gulu la amithenga ochita zoipa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Adagwetsa moto wa ukali wake pa iwo: adaŵapsera mtima naŵakwiyira nkuŵagwetsera mavuto. Zimenezi zinali ngati gulu la angelo oononga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Anakhuthula moto wa ukali wake pa iwo, anawapsera mtima nawakwiyira nʼkuwabweretsera masautso. Zimenezi zinali ngati gulu la angelo osakaza. Onani mutuwo |