Masalimo 78:48 - Buku Lopatulika48 Naperekanso zoweta zao kwa matalala, ndi ng'ombe zao kwa mphezi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Naperekanso zoweta zao kwa matalala, ndi ng'ombe zao kwa mphezi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Adalola kuti ng'ombe zao zife ndi matalala ndi kuti nkhosa zao zife ndi zing'aning'ani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Iye anapereka ngʼombe zawo ku matalala, zoweta zawo ku zingʼaningʼani. Onani mutuwo |