Masalimo 78:43 - Buku Lopatulika43 Amene anaika zizindikiro zake mu Ejipito, ndi zodabwitsa zake kuchidikha cha Zowani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Amene anaika zizindikiro zake m'Ejipito, ndi zodabwitsa zake kuchidikha cha Zowani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 pamene Iye adachita zizindikiro zamphamvu ku Ejipito, ndiponso zozizwitsa zake ku dera la ku Zowani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 tsiku limene Iyeyo anaonetsa poyera zizindikiro zozizwitsa zake mu Igupto, zozizwitsa zake mʼchigawo cha Zowani. Onani mutuwo |