Masalimo 78:42 - Buku Lopatulika42 Sanakumbukire dzanja lake, tsikuli anawaombola kwa msautsi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 Sanakumbukire dzanja lake, tsikuli anawaombola kwa msautsi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 Sadakumbukire mphamvu zake kapena tsiku limene adaŵaombola kwa adani ao, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Sanakumbukire mphamvu zake, tsiku limene Iye anawawombola kwa ozunza, Onani mutuwo |