Masalimo 78:40 - Buku Lopatulika40 Kawirikawiri nanga anapikisana ndi Iye kuchigwako, nammvetsa chisoni m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 Kawirikawiri nanga anapikisana ndi Iye kuchigwako, nammvetsa chisoni m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Kaŵirikaŵiri ankamuukira m'chipululu, ankamumvetsa chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Nthawi zambiri iwo ankamuwukira Iye mʼchipululu ndi kumumvetsa chisoni mʼdziko lopanda kanthu! Onani mutuwo |