Masalimo 78:39 - Buku Lopatulika39 Ndipo anakumbukira kuti iwo ndiwo anthu; mphepo yopita yosabweranso. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 Ndipo anakumbukira kuti iwo ndiwo anthu; mphepo yopita yosabweranso. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Ankakumbukira kuti iwo anali anthu chabe, ngati mphepo yopita imene siibwereranso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Iye anakumbukira kuti iwo anali anthu chabe, mphepo yopita imene sibwereranso. Onani mutuwo |