Masalimo 78:34 - Buku Lopatulika34 Pamene anawapha ndipo anamfuna Iye; nabwerera, nafunitsitsa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Pamene anawapha ndipo anamfuna Iye; nabwerera, nafunitsitsa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Pamene ankapha ena, otsalira ankayamba kumufunafuna. Ankalapa namafunafuna Mulungu ndi mtima wao wonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Mulungu atawapha, iwo amamufunafuna Iyeyo; iwo ankatembenukiranso kwa Iye mwachangu. Onani mutuwo |