Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 78:29 - Buku Lopatulika

29 Potero anadya nakhuta kwambiri; ndipo anawapatsa chokhumba iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Potero anadya nakhuta kwambiri; ndipo anawapatsa chokhumba iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Motero adadya nakhuta kwambiri, popeza kuti adaŵapatsa zakudya zimene ankakhumba.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Iwo anadya mpaka anatsala nazo zochuluka pakuti Iye anawapatsa zimene anazilakalaka.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 78:29
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anawapatsa chopempha iwo; koma anaondetsa mitima yao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa