Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 78:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo anawavumbitsira nyama ngati fumbi, ndi mbalame zouluka ngati mchenga wa kunyanja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo anawavumbitsira nyama ngati fumbi, ndi mbalame zouluka ngati mchenga wa kunyanja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Adaŵagwetsera nyama yochuluka ngati fumbi, mbalame zochuluka ngati mchenga wakunyanja.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Iye anawagwetsera nyama ngati fumbi, mbalame zowuluka ngati mchenga wa mʼmbali mwa nyanja.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 78:27
4 Mawu Ofanana  

Ndipo kudachokera mphepo kwa Yehova, n'kudza nazo zinziri zochokera kunyanja, ndipo zidagwa kuchigono, ulendo wa tsiku limodzi dera lino, ndi ulendo wa tsiku limodzi dera lina, pozungulira pa chigono, ndipo zinabisa nthaka ngati muyeso wa mikono iwiri.


Ndipo anthu anauka tsiku lonselo, ndi usiku wake wonse, ndi mawa lake lonse, nakusa zinzirizo; wokusa pang'ono anakusa zodzaza mahomeri khumi; ndipo anadziyanikira izi pozungulira pa chigono.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa