Masalimo 78:21 - Buku Lopatulika21 Chifukwa chake Yehova anamva, nakwiya; ndipo anayatsa moto pa Yakobo, ndiponso mkwiyo unakwera pa Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Chifukwa chake Yehova anamva, nakwiya; ndipo anayatsa moto pa Yakobo, ndiponso mkwiyo unakwera pa Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Nchifukwa chake Chauta atamva zimenezi, adapsa mtima kwambiri, adayatsira moto Yakobe, napambana kukwiyira Israeleyo, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Yehova atawamva anakwiya kwambiri; moto wake unayaka kutsutsana ndi Yakobo, ndipo mkwiyo wake unauka kutsutsana ndi Israeli, Onani mutuwo |