Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 78:20 - Buku Lopatulika

20 Taonani, anapanda thanthwe, ndi madzi anayendako ndi mitsinje inasefuka; kodi adzakhozanso kupatsa mkate? Kodi adzafunira anthu ake nyama?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Taonani, anapanda thanthwe, ndi madzi anayendako ndi mitsinje inasefuka; kodi adzakhozanso kupatsa mkate? Kodi adzafunira anthu ake nyama?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Paja adamenya thanthwe, kotero kuti madzi adatumphuka, ndipo mitsinje idadzaza. Kodi angathenso kutipatsa ife anthu ake buledi kapena kutipezera nyama?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Iye atamenya thanthwe madzi anatuluka, ndipo mitsinje inadzaza ndi madzi. Koma iye angatipatsenso ife chakudya? Kodi angapereke nyama kwa anthu akewa?”

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 78:20
7 Mawu Ofanana  

Pakuti anabwerera m'mbuyo, nayesa Mulungu, nachepsa Woyerayo wa Israele.


Ndipo unene ndi anthu, Mudzipatuliretu, mawa mudzadya nyama; popeza mwalira m'makutu a Yehova, ndi kuti, Adzatipatsa nyama ndani? Popeza tinakhala bwino mu Ejipito. Potero Yehova adzakupatsani nyama, ndipo mudzadya.


Ndipo anthu osokonezeka ali pakati pao anagwidwa nacho chilakolako; ndi ana a Israele omwe analiranso, nati, Adzatipatsa nyama ndani?


Ndipo Mose anasamula dzanja lake, napanda thanthwe kawiri ndi ndodo; ndipo madzi anatulukamo ochuluka, ndi khamulo linamwa, ndi zoweta zao zomwe.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa