Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 77:19 - Buku Lopatulika

19 Njira yanu inali m'nyanja, koyenda Inu nkumadzi aakulu, ndipo mapazi anu sanadziwike.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Njira yanu inali m'nyanja, koyenda Inu nku madzi aakulu, ndipo mapazi anu sanadziwike.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Inu mudadzera pa nyanja, njira yanu idadzera pa madzi akuya, komabe mapazi anu sadaoneke.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Njira yanu inadutsa pa nyanja, njira yanu inadutsa pa madzi amphamvu, ngakhale zidindo za mapazi anu sizinaoneke.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 77:19
13 Mawu Ofanana  

Pomwepo dziko linagwedezeka ndi kunthunthumira. Maziko a dziko la kumwamba anasunthika. Nagwedezeka, chifukwa Iye anakwiya.


Ndipo munagawanitsa nyanja pamaso pao, napita iwo pakati pa nyanja pouma, ndipo munaponya mozama owalondola, ngati mwala m'madzi olimba.


Pakuti adzachita chondiikidwiratu; ndipo zambiri zotere zili ndi Iye.


Pali munthu kodi wodziwitsa mayalidwe a mitambo, ndi kugunda kwa msasa wake?


amene apenyerera padziko lapansi, ndipo linjenjemera; akhudza mapiri, ndipo afuka.


Yehova anakhala pa chigumula, inde Yehova akhala mfumu kunthawi yonka muyaya.


Pomzinga pali mitambo ndi mdima; chilungamo ndi chiweruzo ndizo zolimbitsa mpando wake wachifumu.


Mphezi zake zinaunikira dziko lokhalamo anthu; dziko lapansi linaona nilinagwedezeka.


Popeza madziwo anabwerera, namiza magaleta ndi apakavalo, ndiwo nkhondo yonse ya Farao imene idalowa pambuyo pao m'nyanja; sanatsale wa iwowa ndi mmodzi yense.


Ndipo phiri la Sinai linafuka monsemo, popeza Yehova anatsikira m'moto pamenepo; ndi utsi wake unakwera ngati utsi wa m'ng'anjo, ndi phiri lonse linagwedezeka kwambiri.


Munaponda panyanja ndi akavalo anu, madzi amphamvu anaunjikana mulu.


Ha! Kuya kwake kwa kulemera ndi kwa nzeru ndi kwa kudziwa kwake kwa Mulungu! Osasanthulikadi maweruzo ake, ndi njira zake nzosalondoleka!


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa