Masalimo 77:16 - Buku Lopatulika16 Madziwo anakuonani Mulungu; anakuonani madziwo; anachita mantha, zozama zomwe zinanjenjemera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Madziwo anakuonani Mulungu; anakuonani madziwo; anachita mantha, zozama zomwe zinanjenjemera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Pamene madzi adakuwonani, Inu Mulungu, pamene madzi adakuwonani, adachita mantha, inde, nyanja yakuya idanjenjemera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Madzi anakuonani Mulungu, madzi anakuonani ndipo anachita mantha; nyanja yozama inakomoka. Onani mutuwo |