Masalimo 77:14 - Buku Lopatulika14 Inu ndinu Mulungu wakuchita chodabwitsa; munazindikiritsa mphamvu yanu mwa mitundu ya anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Inu ndinu Mulungu wakuchita chodabwitsa; munazindikiritsa mphamvu yanu mwa mitundu ya anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Inu ndinu Mulungu amene mumachita zodabwitsa, amene mwaonetsa mphamvu zanu pakati pa mitundu ya anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Inu ndinu Mulungu wochita zodabwitsa; Mumaonetsera mphamvu yanu pakati pa mitundu ya anthu. Onani mutuwo |