Masalimo 77:13 - Buku Lopatulika13 Mulungu, m'malo opatulika muli njira yanu; Mulungu wamkulu ndani monga Mulungu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Mulungu, m'malo opatulika muli njira yanu; Mulungu wamkulu ndani monga Mulungu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Njira zanu, Inu Mulungu, nzoyera. Kodi alipo mulungu winanso wamkulu ngati Mulungu wathu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Njira zanu Mulungu ndi zoyera. Kodi ndi mulungu uti ali wamkulu kuposa Mulungu wathu? Onani mutuwo |