Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 75:9 - Buku Lopatulika

9 Koma ine ndidzalalikira kosalekeza, ndidzaimbira zomlemekeza Mulungu wa Yakobo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Koma ine ndidzalalikira kosalekeza, ndidzaimbira zomlemekeza Mulungu wa Yakobo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Koma ine sindidzaleka kukondwera, ndidzaimba nyimbo zotamanda Mulungu wa Yakobe mpaka muyaya.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Kunena za ine, ndidzalengeza izi kwamuyaya; ndidzayimba matamando kwa Mulungu wa Yakobo.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 75:9
8 Mawu Ofanana  

Aone yekha chionongeko chake m'maso mwake, namwe mkwiyo wa Wamphamvuyonse.


Ndidzaimbira Yehova m'moyo mwanga: ndidzaimbira Mulungu wanga zomlemekeza pokhala ndilipo.


Chilungamo chanu sindinachibise m'kati mwamtima mwanga; chikhulupiriko chanu ndi chipulumutso chanu ndinachinena; chifundo chanu ndi choonadi chanu sindinachibisire msonkhano waukulu.


Kuti okondedwa anu alanditsidwe, pulumutsani ndi dzanja lanu lamanja, ndipo mutivomereze.


Kuti ndibukitse lemekezo lanu lonse; pa bwalo la mwana wamkazi wa Ziyoni, ndidzakondwera nacho chipulumutso chanu.


Pakuti Yehova, Mulungu wa Israele, atero kwa ine, Tenga chikho cha vinyo wa ukaliwu padzanja langa, ndi kumwetsa mitundu yonse, imene ndikutumizirako.


Udzamwa ichi ndi kugugudiza, ndi kuchechetachecheta zibade zake, ndi kung'amba mawere ako; pakuti ndachinena, ati Ambuye Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa