Masalimo 75:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti Mulungu ndiye woweruza; achepsa wina, nakuza wina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti Mulungu ndiye woweruza; achepsa wina, nakuza wina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Koma ndi Mulungu yekha amene amagamula milandu, amatsitsa wina, nakweza wina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Koma ndi Mulungu amene amaweruza: Iyeyo amatsitsa wina, nakwezanso wina. Onani mutuwo |