Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 75:6 - Buku Lopatulika

6 Pakuti kukuzaku sikuchokera kum'mawa, kapena kumadzulo, kapena kuchipululu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Pakuti kukuzaku sikuchokera kum'mawa, kapena kumadzulo, kapena kuchipululu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 Kugamula milandu sikuchokeratu kuvuma kapena kuzambwe, ndiponso sikuchokera ku chipululu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 Kugamula milandu sikuchokera kummawa kapena kumadzulo kapena ku chipululu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 75:6
4 Mawu Ofanana  

Amthamangira Iye mwaliuma, ndi zikopa zake zochindikira.


Ndipo Inu Yehova, ndinu chikopa changa; ulemerero wanga, ndi wondiweramutsa mutu wanga.


Achita ufumu mwa mphamvu yake kosatha; maso ake ayang'anira amitundu; opikisana ndi Iye asadzikuze.


Ine ndidziwa mkwiyo wake, ati Yehova, kuti uli chabe; zonyenga zake sizinachite kanthu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa