Masalimo 75:5 - Buku Lopatulika5 musamakwezetsa nyanga yanu; musamalankhula ndi khosi louma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 musamakwezetsa nyanga yanu; musamalankhula ndi khosi louma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Musadzikuze chifukwa cha mphamvu zanu, kapena kumalankhula zamwano.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Musatukule nyanga zanu motsutsana ndi kumwamba; musayankhule ndi khosi losololoka.’ ” Onani mutuwo |