Masalimo 75:4 - Buku Lopatulika4 Ndinati kwa odzitamandira, musamachita zodzitamandira; ndi kwa oipa, Musamakweza nyanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndinati kwa odzitamandira, musamachita zodzitamandira; ndi kwa oipa, Musamakweza nyanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Ndimauza anthu odzitama kuti, “Musadzitame,” ndiponso anthu oipa kuti, “Musadzitukumule chifukwa cha mphamvu zanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kwa odzitama ndikuti, ‘Musadzitamenso,’ ndipo kwa oyipa, ‘Musatukulenso nyanga zanu. Onani mutuwo |