Masalimo 73:27 - Buku Lopatulika27 Pakuti, taonani, iwo okhala patali ndi Inu adzaonongeka; muononga onse akupembedza kwina, kosiyana ndi Inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Pakuti, taonani, iwo okhala patali ndi Inu adzaonongeka; muononga onse akupembedza kwina, kosiyana ndi Inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Onse amene ali kutali ndi Inu adzaonongeka, Inu mumaŵaononga amene ali osakhulupirika kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Iwo amene ali kutali ndi Inu adzawonongeka; Inu mumawononga onse osakhulupirika pamaso panu. Onani mutuwo |