Masalimo 73:19 - Buku Lopatulika19 Ha? M'kamphindi ayesedwa bwinja; athedwa konse ndi zoopsa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ha? M'kamphindi ayesedwa bwinja; athedwa konse ndi zoopsa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Adzangoferatu ndi mantha, ndi kuwonongeka pa kamphindi kochepa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Mwamsangamsanga iwo amawonongedwa, amasesedwa kwathunthu ndi mantha! Onani mutuwo |