Masalimo 68:34 - Buku Lopatulika34 Vomerezani kuti mphamvu nja Mulungu; ukulu wake uli pa Israele, ndi mphamvu yake m'mitambo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Vomerezani kuti mphamvu nja Mulungu; ukulu wake uli pa Israele, ndi mphamvu yake m'mitambo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Vomerezani kuti Mulungu ndi wamphamvu, ulamuliro wake uli pa Israele, mphamvu zake zili mu mlengalenga. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Lengezani za mphamvu za Mulungu, amene ulemerero wake uli pa Israeli amene mphamvu zake zili mʼmitambo. Onani mutuwo |