Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 68:31 - Buku Lopatulika

31 Akulu adzafumira ku Ejipito; Kusi adzafulumira kutambalitsa manja ake kwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Akulu adzafumira ku Ejipito; Kusi adzafulumira kutambalitsa manja ake kwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Akazembe adzabwera kuchokera ku Ejipito. A ku Etiopiya adzafulumira kugonjera Mulungu pokweza manja ao kwa Iye.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Nthumwi zidzachokera ku Igupto; Kusi adzadzipereka yekha kwa Mulungu.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 68:31
11 Mawu Ofanana  

Ndipo Solomoni anaimirira ku guwa la nsembe la Yehova pamaso pa msonkhano wonse wa Israele, natambasulira manja ake kumwamba, nati,


Nditambalitsira manja anga kwa Inu: Moyo wanga ulira Inu monga dziko lolira mvula.


Tikadaiwala dzina la Mulungu wathu, ndi kutambasulira manja athu kwa mulungu wachilendo;


Diso langa lapuwala chifukwa cha kuzunzika kwanga: Ndimaitana Inu, Yehova, tsiku lonse; nditambalitsira manja anga kwa Inu.


Atero Yehova, Ntchito ya Ejipito, ndi malonda a Kusi, ndi a Seba, amuna amsinkhu adzakugonjera, nadzakhala ako; nadzakutsata pambuyo m'maunyolo; adzakugonjera, nadzakugwira; adzakupembedza ndi kunena, Zoona Mulungu ali mwa iwe; ndipo palibenso wina, palibe Mulungu.


Ndipo ndidzaika chizindikiro pakati pao, ndipo ndidzatumiza onse amene apulumuka mwa iwo kwa amitundu, kwa Tarisisi, kwa Puti ndi kwa Aludi, okoka uta kwa Tubala ndi Yavani, kuzisumbu zakutali, amene sanamve mbiri yanga, ngakhale kuona ulemerero wanga; ndipo adzabukitsa ulemerero wanga pakati pa amitundu.


Kuchokera tsidya lija la mitsinje ya Kusi ondipembedza, ndiwo mwana wamkazi wa obalalika anga, adzabwera nacho chopereka changa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa