Masalimo 68:29 - Buku Lopatulika29 Chifukwa cha Kachisi wanu wa mu Yerusalemu mafumu adzabwera nacho chaufulu kukupatsani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Chifukwa cha Kachisi wanu wa m'Yerusalemu mafumu adzabwera nacho chaufulu kukupatsani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Chifukwa cha Nyumba yanu ya ku Yerusalemu, mafumu amabwera ndi mphatso kwa Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Chifukwa cha Nyumba yanu ku Yerusalemu, mafumu adzabweretsa kwa Inu mphatso. Onani mutuwo |