Masalimo 68:25 - Buku Lopatulika25 Oimbira anatsogolera, oimba zoimba anatsata m'mbuyo, pakatipo anamwali oimba mangaka. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Oimbira anatsogolera, oimba zoimba anatsata m'mbuyo, pakatipo anamwali oimba mangaka. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Oimba nyimbo zapakamwa atatsogola, oimba ndi zipangizo ali pambuyo, anamwali oimba ting'oma ali pakati. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Patsogolo pali oyimba nyimbo pakamwa, pambuyo pawo oyimba nyimbo ndi zipangizo; pamodzi ndi iwo pali atsikana akuyimba matambolini. Onani mutuwo |