Masalimo 68:23 - Buku Lopatulika23 kuti uviike phazi lako m'mwazi, kuti malilime a agalu ako alaweko adani ako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 kuti uviike phazi lako m'mwazi, kuti malilime a agalu ako alaweko adani ako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 kuti musambe mapazi anu m'magazi, kuti agalu anu anyambiteko magazi a adaniwo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Kuti muviyike mapazi anu mʼmagazi a adani anu, pamene malilime a agalu anu akudyapo gawo lawo.” Onani mutuwo |