Masalimo 68:22 - Buku Lopatulika22 Ambuye anati, Ndidzawatenganso ku Basani, ndidzawatenganso kozama kwa nyanja, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ambuye anati, Ndidzawatenganso ku Basani, ndidzawatenganso kozama kwa nyanja, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ambuye adati, “Ndidzaŵabweza adani anu kuchokera ku Basani, ndidzaŵabweza kuchokera ku nyanja yozama, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ambuye akunena kuti, “Ndidzawabweretsa kuchokera ku Basani; ndidzawabweretsa kuchokera ku nyanja zozama. Onani mutuwo |