Masalimo 68:14 - Buku Lopatulika14 Pamene Wamphamvuyonse anabalalitsa mafumu m'dzikomo, munayera ngati matalala mu Zalimoni. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Pamene Wamphamvuyonse anabalalitsa mafumu m'dzikomo, munayera ngati matalala m'Zalimoni. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pamene Mphambe adabalalitsa mafumu kumeneko, ku Zalimoni kudagwa chisanu choopsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Pamene Wamphamvuzonse anabalalitsa mafumu mʼdziko, zinali ngati matalala akugwa pa Zalimoni. Onani mutuwo |