Masalimo 65:7 - Buku Lopatulika7 Amene atontholetsa kukuntha kwa nyanja, kukuntha kwa mafunde ake, ndi phokoso la mitundu ya anthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Amene atontholetsa kukuntha kwa nyanja, kukuntha kwa mafunde ake, ndi phokoso la mitundu ya anthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu mumachititsa bata mkokomo wa nyanja ndi mkokomo wa mafunde ndi phokoso la mitundu ina ya anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Amene munakhalitsa bata nyanja kukokoma kwa mafunde ake, ndi phokoso la anthu a mitundu ina. Onani mutuwo |