Masalimo 65:5 - Buku Lopatulika5 Mudzatiyankha nazo zoopsa m'chilungamo, Mulungu wa chipulumutso chathu; ndinu chikhulupiriko cha malekezero onse a dziko lapansi, ndi cha iwo okhala kutali kunyanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mudzatiyankha nazo zoopsa m'chilungamo, Mulungu wa chipulumutso chathu; ndinu chikhulupiriko cha malekezero onse a dziko lapansi, ndi cha iwo okhala kutali kunyanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono Inu mumatiyankha potipulumutsa ndi ntchito zanu zodabwitsa, Inu Mulungu Mpulumutsi wathu. Anthu a pa dziko lonse lapansi ndiponso a patsidya pa nyanja zakutali, onsewo amakhulupirira Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mumatiyankha ife ndi ntchito zodabwitsa zachilungamo, Inu Mulungu Mpulumutsi wathu, chiyembekezo cha mathero onse a dziko lapansi ndi cha nyanja zomwe zili kutali kwambiri, Onani mutuwo |
Ndipo ndidzaika chizindikiro pakati pao, ndipo ndidzatumiza onse amene apulumuka mwa iwo kwa amitundu, kwa Tarisisi, kwa Puti ndi kwa Aludi, okoka uta kwa Tubala ndi Yavani, kuzisumbu zakutali, amene sanamve mbiri yanga, ngakhale kuona ulemerero wanga; ndipo adzabukitsa ulemerero wanga pakati pa amitundu.