Masalimo 65:12 - Buku Lopatulika12 Akukha pa mabusa a m'chipululu; ndipo mapiri azingika nacho chimwemwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Akukha pa mabusa a m'chipululu; ndipo mapiri azingika nacho chimwemwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ngakhale ku mabusa akuchipululu kumamera msipu wambiri, ndipo mapiri amadzazidwa ndi chimwemwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Malo a udzu a mʼchipululu amasefukira; mapiri avekedwa ndi chisangalalo. Onani mutuwo |