Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 65:10 - Buku Lopatulika

10 Mukhutitsa nthaka yake yolima; mufafaniza nthumbira zake; muiolowetsa ndi mvumbi; mudalitsa mmera wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Mukhutitsa nthaka yake yolima; mufafaniza nthumbira zake; muiolowetsa ndi mvumbi; mudalitsa mmera wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Inu mumathirira kwambiri makwaŵa am'mizere, mumasalaza nthumbira zake, mumafeŵetsa nthaka ndi mvula, ndipo mumadalitsa mbeu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Mwadzaza nthaka yake ndi madzi ndi kusalaza migula yake, mwayifewetsa ndi mvula yamawawa ndi kudalitsa mbewu zake.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 65:10
7 Mawu Ofanana  

ngati aufikitsira dziko lake kulidzudzula, kapena kulichitira chifundo.


Iye amwetsa mapiri mochokera m'zipinda zake: Dziko lakhuta zipatso za ntchito zanu.


Amene aphimba thambo ndi mitambo, amene akonzera mvula nthaka, amene aphukitsa msipu pamapiri.


Gulu lanu linakhala m'dziko muja. Mwa ukoma wanu munalikonzera ozunzika, Mulungu.


ndidzakupatsani mvula m'nyengo zake, ndi dziko lidzapereka zipatso zake, ndi mitengo ya m'minda idzabala zipatso zake.


Chiphunzitso changa chikhale ngati mvula; maneno anga agwe ngati mame; ngati mvula yowaza pamsipu, ndi monga madontho a mvula pazitsamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa