Masalimo 63:9 - Buku Lopatulika9 Koma iwo amene afuna moyo wanga kuti auononge, adzalowa m'munsi mwake mwa dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma iwo amene afuna moyo wanga kuti auononge, adzalowa m'munsi mwake mwa dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Koma anthu amene amayesayesa kuwononga moyo wanga, adzatsikira ku dziko la anthu akufa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Iwo amene akufunafuna moyo wanga adzawonongedwa; adzatsikira kunsi kozama kwa dziko lapansi. Onani mutuwo |