Masalimo 63:8 - Buku Lopatulika8 Moyo wanga uumirira Inu. Dzanja lamanja lanu lindigwiriziza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Moyo wanga uumirira Inu. Dzanja lamanja lanu lindigwiriziza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mtima wanga ukukangamira Inu, dzanja lanu lamanja likundichirikiza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Moyo wanga umakangamira Inu; dzanja lanu lamanja limandigwiriziza. Onani mutuwo |