Masalimo 63:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti munakhala mthandizi wanga; ndipo ndidzafuula mokondwera mu mthunzi wa mapiko anu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti munakhala mthandizi wanga; ndipo ndidzafuula mokondwera mu mthunzi wa mapiko anu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu mwakhala chithandizo changa, motero ndikuimba ndi chimwemwe pansi pa mapiko anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Chifukwa ndinu thandizo langa, ine ndimayimba mu mthunzi wa mapiko anu. Onani mutuwo |