Masalimo 63:6 - Buku Lopatulika6 Pokumbukira Inu pa kama wanga, ndi kulingalira za Inu maulonda a usiku. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Pokumbukira Inu pa kama wanga, ndi kulingalira za Inu maulonda a usiku. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndikagona pabedi panga ndimalingalira za Inu, usiku wonse ndimasinkhasinkha za Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Pa bedi panga ndimakumbukira inu; ndimaganiza za Inu nthawi yonse ya usiku. Onani mutuwo |