Masalimo 63:5 - Buku Lopatulika5 Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi zonona; ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakufuula mokondwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mudzakhutitsa moyo wanga ngati ndi mafuta ndi chonona; ndipo pakamwa panga ndidzakulemekezani ndi milomo yakufuula mokondwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mudzandikhutitsa ndi zonona, ndipo ndidzakutamandani ndi mau osangalala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mudzakhutitsa moyo wanga ndi zonona. Ine ndidzakutamandani ndi mawu anthetemya. Onani mutuwo |