Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Masalimo 63:4 - Buku Lopatulika

4 Potero ndidzakuyamikani m'moyo mwanga; ndidzakweza manja anga m'dzina lanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Potero ndidzakuyamikani m'moyo mwanga; ndidzakweza manja anga m'dzina lanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Choncho ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga. Ndidzakweza manja anga kwa Inu mopemphera.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Ndidzakutamandani masiku onse a moyo wanga, ndipo mʼdzina lanu ndidzakweza manja anga.

Onani mutuwo Koperani




Masalimo 63:4
7 Mawu Ofanana  

Ndidzaimbira Yehova m'moyo mwanga: ndidzaimbira Mulungu wanga zomlemekeza pokhala ndilipo.


Kwezani manja anu kumalo oyera, nimulemekeze Yehova.


Mverani mau a kupemba kwanga, pamene ndilirira Inu, pamene ndikweza manja anga kuloza ponenera panu poyera.


Mapiri anakuonani, namva zowawa; chigumula cha madzi chinapita; madzi akuya anamveketsa mau ake, nakweza manja ake m'mwamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa